Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,

 

YESU ndiye Mbuye wanga,
Ndamva mawu akewo;
Anandilandira ine,
Nandipulumutsatu.

Mwalembedwa mukalata,
Mawu ake omwewo;
Kuti iwo akumvera,
Akalandiridwatu.

Ndinakhala woipadi,
Ndinam’kana kalelo;
Koma Yesu waiwala,
Mphulupulu zangazo.

Wapumitsa mtima wanga,
Kaamba ndaphunziratu;
Mawu ake olembedwa,
Mukalata mwakemo.

Mumvetu abwenzi athu,
Musakanilire’yi;
Yesu ayitana inu,
Zalembedwa zomwezi.

Post navigation

Previous: Hymn 239 TILI ndi mtendere
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version