Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 238 MULUNGU wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 238 MULUNGU wanga,

Hymn 238 MULUNGU wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 238 MULUNGU wanga,

 

MULUNGU wanga,
Ndapeza moyo;
Ndili wokondwera
Masiku onse.

Aleluya, muyenera!
Aleluya, Amen.
Aleluya, ndidzamtama
Mulungu wanga.

Mwazi wa Yesu
Unditsukatu,
Ndiye Mbuye wanga
Ndi Mpulumutsi.

Pamtanda wake ’Nafera ine,
Ndi zoipa zanga ’Nazichotsadi.

Mulungu wanga
Andilandira,
Chifukwa cha Yesu
Mwana wakeyo.

Adzabweranso
Kundilandira
Ndikhale ndi Iye
Masiku onse.

Post navigation

Previous: Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
Next: Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version