Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

 

ZAMBIRI zogona m’kholamo,
Zosungika bwino ’mo;
Koma imodzi inasokeradi,
Nitayika m’thengomo
Kutali kuphiri loopsalo,
Kutali ndi mbusa wakeyo.

Ambuye, muli nazo zambirizi,
Kodi sizifikirazi?
Koma Mbusa nanena, “Yangayo
Yatayika naneyo;
Ngakhale njira njoopsadi,
Ndilinga kuphiri kuipezanso.”

Koma zina sizinadziŵa ayi,
Makwaŵa ’napyola ’Ye,
Ndi mdima woopsa wa usikuwo
Ambuye nailonda yake.
Anamva kulira kutaliko,
Naipeza yofoka, yakufayo.

Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
Panjira ponsepo?
“Ndaukhetsa potsata iwetu,
Kukubweza ku kholalo.”
Ndi m’manja mwalaswa bwanjimo?
“Ndalaswa ndi minga pofuna iwe.”

Ndi ponse paphiri ndi padambopo
Ndi makwaŵa, indetu,
Kunakwera kupfuula Kumwambako,
“Kondwani, ndaipeza yanga!”
Nd’ angelo a Mlungu nabwezanso,
“Kondwani, Ambuye ’napeza yawo.”

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version