Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

 

ZAMBIRI zogona m’kholamo,
Zosungika bwino ’mo;
Koma imodzi inasokeradi,
Nitayika m’thengomo
Kutali kuphiri loopsalo,
Kutali ndi mbusa wakeyo.

Ambuye, muli nazo zambirizi,
Kodi sizifikirazi?
Koma Mbusa nanena, “Yangayo
Yatayika naneyo;
Ngakhale njira njoopsadi,
Ndilinga kuphiri kuipezanso.”

Koma zina sizinadziŵa ayi,
Makwaŵa ’napyola ’Ye,
Ndi mdima woopsa wa usikuwo
Ambuye nailonda yake.
Anamva kulira kutaliko,
Naipeza yofoka, yakufayo.

Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
Panjira ponsepo?
“Ndaukhetsa potsata iwetu,
Kukubweza ku kholalo.”
Ndi m’manja mwalaswa bwanjimo?
“Ndalaswa ndi minga pofuna iwe.”

Ndi ponse paphiri ndi padambopo
Ndi makwaŵa, indetu,
Kunakwera kupfuula Kumwambako,
“Kondwani, ndaipeza yanga!”
Nd’ angelo a Mlungu nabwezanso,
“Kondwani, Ambuye ’napeza yawo.”

Post navigation

Previous: Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Next: Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version