Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
Next: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version