Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version