Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
Next: Hymn 112 ELISA mneneri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version