Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version