Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

 

NDI mitima yokondwera,
Mbuye wathu tiyamika.

E, chifundo chake chonse,
Ndi chosatha nthaŵi zonse.

Dzina lake tibukitsa,
Mlungu ndiye yekhayekha.

Mphamvu yake inalenga,
Dziko lonse ndi kumwamba.

Anatsogolera kale,
M’chipululu anthu ake.

Ndi chifundo atipenya,
Ife anthu osawuka.

Amaŵeta nyama zonse,
Zingasoŵe kanthu konse.

Tiimbire Mlungu wathu,
Waulemu ndi wamkulu.

Tithaŵire kwa Mulungu,
Ndiko tikapeze moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 10 TSOPANO linoli,
Next: Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version