Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 11 NDI mitima yokondwera,

 

NDI mitima yokondwera,
Mbuye wathu tiyamika.

E, chifundo chake chonse,
Ndi chosatha nthaŵi zonse.

Dzina lake tibukitsa,
Mlungu ndiye yekhayekha.

Mphamvu yake inalenga,
Dziko lonse ndi kumwamba.

Anatsogolera kale,
M’chipululu anthu ake.

Ndi chifundo atipenya,
Ife anthu osawuka.

Amaŵeta nyama zonse,
Zingasoŵe kanthu konse.

Tiimbire Mlungu wathu,
Waulemu ndi wamkulu.

Tithaŵire kwa Mulungu,
Ndiko tikapeze moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version