Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
Next: Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version