Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version