Hymn 50 Akhristu nyamulani December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Believers Christian Hymns Chichewa Believers Christian Hymns Hymn 50 Akhristu nyamulani Akhristu nyamulani Maneno a Mulungu, Ndi moyo lalikani Pa dziko lonselo; Ndi Yesu Mpulumutsi Anatiferatu; Adzabvomera onse: Ndi Mwana wa Mlungu.