Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 50 Akhristu nyamulani
Akhristu nyamulani
Maneno a Mulungu,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse:
Ndi Mwana wa Mlungu.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 50 Akhristu nyamulani
Akhristu nyamulani
Maneno a Mulungu,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse:
Ndi Mwana wa Mlungu.