Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 50 Akhristu nyamulani

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 50 Akhristu nyamulani

 

Akhristu nyamulani

Maneno a Mulungu,

Ndi moyo lalikani

Pa dziko lonselo;

Ndi Yesu Mpulumutsi

Anatiferatu;

Adzabvomera onse:

Ndi Mwana wa Mlungu.

Exit mobile version