Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

 

MLUNGU, Inutu,
Mwalenga dzuŵali,
Nyenyezi, mwezi mbee,
Ndi dzikoli.

Koma ineyu
Simuiŵala ’yi;
Mundisamala ’ne
Ndisagwe ’yi.

Mbuye, Msungi ’Nu,
Mutuma indedi
Za moyo wangawu
Zokomazi.

Yesu Mwanatu
Anafa imfayo
Achotsa zoti bii;
Nadzukanso;

Kuti m’Mwambamo
Ndikatamandetu
Wondisamalabe,
Mbuyangayu.

Post navigation

Previous: Hymn 451 MLUNGU alinane;
Next: Hymn 453 A! MULUNGU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version