Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 450 YESU, munditsogoza

  1. Home   »  
  2. Hymn 450 YESU, munditsogoza

Hymn 450 YESU, munditsogoza

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 450 YESU, munditsogoza

 

YESU, munditsogoza
M’njira yanga yonseyo;
Wakunditsogozatu
Ndinu, mundisungetu;
Inde, paulendowo
Mundisunge kolimba.

Monga may’asusunza
Mwana wake polira,
Wakunditonthozatu
Ndinu, munditonthoze,
Ine, m’njira yanuyi
Munditsogoleretu.

Mbuye, ndinu wamphamvu,
Mumatola ananu.
Anthu onse pansipa
Ali otaikatu;
Muchitire chifundo,
Muŵatole onsewo.

Post navigation

Previous: Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
Next: Hymn 451 MLUNGU alinane;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version