Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

  1. Home   »  
  2. Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!

 

ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
Ambuye wa Kumwambako aloŵe momwemo.

Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
Kufana ndi nyenyezi younika m’mdimamo.

Ankondo a Mulungu ’nu,
Yendani m’njiramo,
Mitima yanu yonseyo iyeretsedwe mbuu!

Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
Mlaliketu Uthenga kwa anthu onsewo.

Musamaopa kanthu ’yi tamani Yesuyo;
Kaimbireni nyimboyi ndi mphamvu zonse.

Zipata zatsegudwa mbee! za m’dziko monsemo;
Ambuye wapambanatu ndi mtanda wakewo.

Post navigation

Previous: Hymn 412 MOYO uli pafupi,
Next: Hymn 414 INU bambo, inu mayi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version