Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

 

NJIRA yanga sindiziŵa,
’Tate muikonza;
Komatu muzindikira
Kuti mundikonda.

M’mene mantha andigwira,
Andidetsa m’mtima,
Mbuye, ndithaŵire kwanu
Poti mundikonda.

Sindidziŵatu zamaŵa,
Koma sindiopa;
Ndidzakhulupira Inu
Kuti mundikonda.

Inde wakukonda ndinu;
Mawuwo oona
Andidzaza ndi chimwemwe:
Mlungu andikonda.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version