Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

 

MBUYANGA Yesu,
mundigwire dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version