Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

 

MBUYANGA Yesu,
mundigwire dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
Next: Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version