Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

  1. Home   »  
  2. Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

 

MBUYANGA Yesu, mundigwire
Dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
Next: Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version