Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

  1. Home   »  
  2. Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

 

MBUYANGA Yesu, mundigwire
Dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version