Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

 

NDISAUKA, ndinachimwa,
Koma Inu m’nandifera;
Ndimo ndamva mund’itana,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, ndimasowa,
Mphamvu yakuyera m’mtima;
Mwazi wanu wanditsuka,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindikhoza,
Kuiletsa nkhondo m’ mtima;
Ndi chisoni, mantha nkhawa,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Ndisauka, sindiona,
Ndingodwala, ndilefuka;
Zonse ndizitaya kwa ‘Nu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mulandira,
Muchiritsa, m’ pulumutsa;
Mawu anu ndivomera,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Inde, Yesu, mundikonda,
Zonse zina ndazitaya;
Tsono kukhala wanu,
Mwana Mlungu ndingobwera.

Post navigation

Previous: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
Next: Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version