Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

  1. Home   »  
  2. Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

 

NDINASOKERA kutali,
Ndinadya ndi nguluwe,
Ndinakhala mu zoipa,
Chifukwa ndinachimwa.

Mmene ndafika
kwa ‘tate,
Nandikonzeratu phwando;
“Tidye tisekere naye,
Mwanayu anasowa.”

Koma mkulu wanga ndiye,
Sanandirandiretu;
Sanafune tate wanga,
Andikhululukire.

Ambuye amayitana,
Anthu onse ochimwa;
Kuti adzetu kwa Iye,
Kumene kuli moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
Next: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version