Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

  1. Home   »  
  2. Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 199 NDINASOKERA kutali,

 

NDINASOKERA kutali,
Ndinadya ndi nguluwe,
Ndinakhala mu zoipa,
Chifukwa ndinachimwa.

Mmene ndafika
kwa ‘tate,
Nandikonzeratu phwando;
“Tidye tisekere naye,
Mwanayu anasowa.”

Koma mkulu wanga ndiye,
Sanandirandiretu;
Sanafune tate wanga,
Andikhululukire.

Ambuye amayitana,
Anthu onse ochimwa;
Kuti adzetu kwa Iye,
Kumene kuli moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version