Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

 

LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
Musekerere kuti tidzaimbira Yesu.
Imbira!
Timwimbire Yesu,
Mpulumutsi wathu!

Imbira!
Timwimbire Yesu,
Tonse tidzakondwera.

Musadziunjikire chuma cha padziko
Dzimbiri ndi njenjete
zimachiononga.

Koma mudziunjikire chuma cha Kumwamba
Kumene anapita Mtsogoleri wanu.

Aliponso adani am’kati ndi akunja;
Yesu watisekera, tidzakuimbirani.

Aliponse mabvuto, ena ndi oipa;
Yesu mutimasule kwa adani athu.

Post navigation

Previous: Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
Next: Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version