Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

 

ZAMBIRI zogona m’kholamo,
Zosungika bwino ’mo;
Koma imodzi inasokeradi,
Nitayika m’thengomo
Kutali kuphiri loopsalo,
Kutali ndi mbusa wakeyo.

Ambuye, muli nazo zambirizi,
Kodi sizifikirazi?
Koma Mbusa nanena, “Yangayo
Yatayika naneyo;
Ngakhale njira njoopsadi,
Ndilinga kuphiri kuipezanso.”

Koma zina sizinadziŵa ayi,
Makwaŵa ’napyola ’Ye,
Ndi mdima woopsa wa usikuwo
Ambuye nailonda yake.
Anamva kulira kutaliko,
Naipeza yofoka, yakufayo.

Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
Panjira ponsepo?
“Ndaukhetsa potsata iwetu,
Kukubweza ku kholalo.”
Ndi m’manja mwalaswa bwanjimo?
“Ndalaswa ndi minga pofuna iwe.”

Ndi ponse paphiri ndi padambopo
Ndi makwaŵa, indetu,
Kunakwera kupfuula Kumwambako,
“Kondwani, ndaipeza yanga!”
Nd’ angelo a Mlungu nabwezanso,
“Kondwani, Ambuye ’napeza yawo.”

Post navigation

Previous: Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Next: Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version