Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

 

ZAMBIRI zogona m’kholamo,
Zosungika bwino ’mo;
Koma imodzi inasokeradi,
Nitayika m’thengomo
Kutali kuphiri loopsalo,
Kutali ndi mbusa wakeyo.

Ambuye, muli nazo zambirizi,
Kodi sizifikirazi?
Koma Mbusa nanena, “Yangayo
Yatayika naneyo;
Ngakhale njira njoopsadi,
Ndilinga kuphiri kuipezanso.”

Koma zina sizinadziŵa ayi,
Makwaŵa ’napyola ’Ye,
Ndi mdima woopsa wa usikuwo
Ambuye nailonda yake.
Anamva kulira kutaliko,
Naipeza yofoka, yakufayo.

Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
Panjira ponsepo?
“Ndaukhetsa potsata iwetu,
Kukubweza ku kholalo.”
Ndi m’manja mwalaswa bwanjimo?
“Ndalaswa ndi minga pofuna iwe.”

Ndi ponse paphiri ndi padambopo
Ndi makwaŵa, indetu,
Kunakwera kupfuula Kumwambako,
“Kondwani, ndaipeza yanga!”
Nd’ angelo a Mlungu nabwezanso,
“Kondwani, Ambuye ’napeza yawo.”

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version