Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

 

MIPINGO iyo idzatu,
Yoyenda mangu pajapo,
Afuma kuti anthuwo?
Afika bwanji komweko?

Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo.”
Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo”

Azizwa anthu ajawo,
Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.”

Ndi Yesu yemwe kalelo,
’Nakhala munthu pansipa;
Anthenda onsenthaŵiyo
Nachirayake mphamvuyo

Afika Yesu leroli,
Chifundo m’mtima wakemo,
Timfitse msanga kwathuko
Akhale nafe ponsepo.

Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Timyese Mfumu yathuyo,
Chifukwa tikamkanatu
Tikhala otayikawo.

Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo.
Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo

Post navigation

Previous: Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
Next: Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version