Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

 

MIPINGO iyo idzatu,
Yoyenda mangu pajapo,
Afuma kuti anthuwo?
Afika bwanji komweko?

Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo.”
Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo”

Azizwa anthu ajawo,
Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.”

Ndi Yesu yemwe kalelo,
’Nakhala munthu pansipa;
Anthenda onsenthaŵiyo
Nachirayake mphamvuyo

Afika Yesu leroli,
Chifundo m’mtima wakemo,
Timfitse msanga kwathuko
Akhale nafe ponsepo.

Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Timyese Mfumu yathuyo,
Chifukwa tikamkanatu
Tikhala otayikawo.

Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo.
Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version