Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 112 ELISA mneneri,

  1. Home   »  
  2. Hymn 112 ELISA mneneri,

Hymn 112 ELISA mneneri,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 112 ELISA mneneri,

 

ELISA mneneri,
Wachita zamphamvu;
Kuyandamitsa nkhwangwayo,
Pa Yolodani’po.

(M) Nkhwangwayo,
(O) Ndiyobwereka,
Nalira mnyamatayo;
Popeza ndiyobwereka,
Pa Yolodanipo.

Elisa mneneri,
Natenga kamtengo;
Naponya pamadzi paja,
Nkhwangwa niyandama.

Mulungu wamphamvu,
Natuma Mwana ‘ke;
Kuti atifere ife,
Kutipulumutsa.

Nanga ife lero,
Kodi takonzeka;
Kusiya machimo athu,
Kutsata Yesuyo?

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version