Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 112 ELISA mneneri,

  1. Home   »  
  2. Hymn 112 ELISA mneneri,

Hymn 112 ELISA mneneri,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 112 ELISA mneneri,

 

ELISA mneneri,
Wachita zamphamvu;
Kuyandamitsa nkhwangwayo,
Pa Yolodani’po.

(M) Nkhwangwayo,
(O) Ndiyobwereka,
Nalira mnyamatayo;
Popeza ndiyobwereka,
Pa Yolodanipo.

Elisa mneneri,
Natenga kamtengo;
Naponya pamadzi paja,
Nkhwangwa niyandama.

Mulungu wamphamvu,
Natuma Mwana ‘ke;
Kuti atifere ife,
Kutipulumutsa.

Nanga ife lero,
Kodi takonzeka;
Kusiya machimo athu,
Kutsata Yesuyo?

Post navigation

Previous: Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Next: Hymn 113 KALERO anthu onse

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 778 Mwini madalitso,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version