Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

 

PAKWITANA Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku la kuŵalalo,
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Pakuluka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Tisaleke kugwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakondwerera naye komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version