Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

 

PAKWITANA Mbuye wanga
Potsiriza dzikoli,
Pakufika tsiku la kuŵalalo,
Posonkhana akumvera,
Pakuona Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Pakuyiitana Mbuye wanga,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Potuluka m’manda mwawo
Anthu ake onsewo,
Tidzasanganatu nawo nthaŵiyo.
Pakuluka osankhidwa,
Kunka naye Yesuyo,
Ndidzakondwerera naye komweko.

Tisaleke kugwirabe
Ntchito ya Mulunguyo,
Tibukitse mbiri yake m’dzikoli,
Ndi podzatha moyo wathu
Ndi zintchito zathuzo,
Tidzakondwerera naye komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
Next: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 1054 Ndilira mtima wakulapa
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version