Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

 

MMENE Yesu adzabwera,
Adza ndi mitambo;
Ndipo diso lililonse,
Lidzamuwona Iye.

Adza, adza,
Adza ndi mitambo,
Ndipo diso lililonse;
Lidzamuwona Iye.

Adzakhala pa chimpando,
Choweruziracho;
Nadzayamba kuweruza,
Milandu ya anthu’fe.

Angelo ‘dzagwira ntchito,
Yolekanitsadi;
Anthu onse a padziko,
M’magulu awiritu.

Olugama nadzayima,
Kudzanja lamanja;
Koma onse oyipawo,
Mbali yakumanzere.

Akudzanja lamanjalo,
Kumoyo wosatha;
Akudzanja lamanzere,
Kumoto Wosathawo.

Post navigation

Previous: Hymn 76 E, MOYO wanga’we
Next: Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1037 Mapemphero athu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version