Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

 

MMENE Yesu adzabwera,
Adza ndi mitambo;
Ndipo diso lililonse,
Lidzamuwona Iye.

Adza, adza,
Adza ndi mitambo,
Ndipo diso lililonse;
Lidzamuwona Iye.

Adzakhala pa chimpando,
Choweruziracho;
Nadzayamba kuweruza,
Milandu ya anthu’fe.

Angelo ‘dzagwira ntchito,
Yolekanitsadi;
Anthu onse a padziko,
M’magulu awiritu.

Olugama nadzayima,
Kudzanja lamanja;
Koma onse oyipawo,
Mbali yakumanzere.

Akudzanja lamanjalo,
Kumoyo wosatha;
Akudzanja lamanzere,
Kumoto Wosathawo.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version