Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

 

KODI mwaona chiyani,
Anzeru a kummawa?
Nyenyezi’yo yaoneka,
Isonyeza njirayo.

Mtendere padziko lonse,
Mtendere padziko lonse;
Kwa anthu onse amene,
Alandira Yesuyo.

Nyenyeziyo pooneka,
Isonyeza chikondi;
Kuti Yesu wabadwadi,
Mu kholalo la ng’ombe.

Ndipo iye wolandira,
Ambuye wathu Yesu;
Akhalanso nawo zedi,
Moyowo wochuluka.

Post navigation

Previous: Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
Next: Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version