Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

 

YEHOVA, Mbusa wangadi,
Ndilibe kusoŵa;
Andigonetsa bwinoli
Mumsipu wokoma.

Ku madzi ake odikha
Anditsogolera;
Ndi moyo wanga wofoka
Aulimbikitsa.

Anditsogolera m’njira
Zakulungamazo;
Chifukwa changa ay’, koma
Cha dzina lakelo.

Ndipyola kodi chikhwaŵa
Cha mthunzi wa imfa?
Ndilibe mantha ngati ’Nu
Mundiperekeza.

Chakudya changa chabwino
Mwandikonzera pha!
Pamaso pa adaniwo
Mudyetsa mtimanga.

Mwadzoza mutu wanga ndi
Mafuta okoma;
Mwadzadza chikho changadi,
Inde, chisefuka.

Zokoma ndi zakuyanja
Zidzanditsatako;
Ndikhala m’nyumba ya Mlungu
Ku nthaŵi zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version