Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

 

YEHOVA, Mbusa wangadi,
Ndilibe kusoŵa;
Andigonetsa bwinoli
Mumsipu wokoma.

Ku madzi ake odikha
Anditsogolera;
Ndi moyo wanga wofoka
Aulimbikitsa.

Anditsogolera m’njira
Zakulungamazo;
Chifukwa changa ay’, koma
Cha dzina lakelo.

Ndipyola kodi chikhwaŵa
Cha mthunzi wa imfa?
Ndilibe mantha ngati ’Nu
Mundiperekeza.

Chakudya changa chabwino
Mwandikonzera pha!
Pamaso pa adaniwo
Mudyetsa mtimanga.

Mwadzoza mutu wanga ndi
Mafuta okoma;
Mwadzadza chikho changadi,
Inde, chisefuka.

Zokoma ndi zakuyanja
Zidzanditsatako;
Ndikhala m’nyumba ya Mlungu
Ku nthaŵi zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 29 CHIKONDI cha
Next: Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version