Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

  1. Home   »  
  2. Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

 

LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Lemekeza Mulungu Mwana,
Lemekeza Mulungu Mzimu,
Mulungu Mmodzi ndi wamkulu,
Lemekeza, lemekeza
Mulungu wathu yemweyo.

Mlemekeze, anakonda
Natitsuka m’mtima mwathu;
Anatiwombola ife
Tikakhale ndi chifumu.
Lemekeza, lemekeza
Yesu Mbuye Nsembeyo.

Lemekeza Mfumu yathu,
Mfumu ya mipingo yonse,
Ipambana anthu onse
Akumwamba ndi apansi.
Lemekeza, lemekeza
Mfumu ya mafumuyo

Post navigation

Previous: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
Next: Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version