Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 94 KHAMULO liliko

  1. Home   »  
  2. Hymn 94 KHAMULO liliko

Hymn 94 KHAMULO liliko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 94 KHAMULO liliko

 

KHAMULO liliko
Kumwambako mbuu!
Pakukhala ndi Yesu
Aimbirako:

Kwa Iye atikonda
Natsuka ’fe mbuu!
E! kukhale ulemu
Kwa Mbuyathuyu.

Onsewa ’nachimwa
Nadetsedwa bii,
Nthaŵi yino ayera
Naimbiradi:

Akhala mafumu
Kwa Mbuyathuyo,
Anawombola onse
Ndi mwaziwo pyu!

Akadakhalabe
Osaukako
Ngati Yesu sakana
Wombolatuwo.

Ndi nyimbo yabwino
Tidzamtamako,
Kuti ena pakumva
Amuyimbirenso:

Post navigation

Previous: Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
Next: Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version