Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 94 KHAMULO liliko

  1. Home   »  
  2. Hymn 94 KHAMULO liliko

Hymn 94 KHAMULO liliko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 94 KHAMULO liliko

 

KHAMULO liliko
Kumwambako mbuu!
Pakukhala ndi Yesu
Aimbirako:

Kwa Iye atikonda
Natsuka ’fe mbuu!
E! kukhale ulemu
Kwa Mbuyathuyu.

Onsewa ’nachimwa
Nadetsedwa bii,
Nthaŵi yino ayera
Naimbiradi:

Akhala mafumu
Kwa Mbuyathuyo,
Anawombola onse
Ndi mwaziwo pyu!

Akadakhalabe
Osaukako
Ngati Yesu sakana
Wombolatuwo.

Ndi nyimbo yabwino
Tidzamtamako,
Kuti ena pakumva
Amuyimbirenso:

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hello world!
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version