Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

 

TAMANI Ambuye,
Wamphamvu ndi Iye;
Akhala m’ulemu,
Kumwamba komweko.
Chikopa cholimba,
Ndi kothaŵiranso;
Kwa anthu akewo,
Kotero ndi Mlungu.

Uzani zamphamvu,
Imbani chisomo;
Za Mwini ulemu,
Ambuye wathuyo.
Poomba chimphepo
Mvulanso ndi bingu;
Padziko, pathambo,
Akhala ponsepo.

Zozizwa zam’dziko,
Za M’mwamba zonsezi;
Mulungu wamphamvu,
Munalenga zonse;
Muyendetsa mwezi,
Nyenyezi ndi dzuŵa;
Zolengedwa zonse,
Zimvera Ambuye.

Sitiha ifedi,
Kukamba zokoma;
Za Inu Mulungu,
Wolera anthuwa.
Zifika ndi mphepo,
Ndi mvula ndi dzuŵa;
Zigwera ponsepo,
Pa anthu onsewa.

Wamphamvu yosatha,
Chikondichangwiro;
Angelo akonda,
Kutama Mulungu.
Ndiponso ifetu,
Ana ‘nu tonse ‘fe;
Tiimba nyimboyi,
Yotama Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version