Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

 

ALINKUDZA wansoni Munthu,
Wakukhala Kumwamba;
Alinkudza m’ulemerero,
Ndi Mwamuna wa mtanda.

Aleluya, Aleluya,
Alinkudza kwa ife;
Ndi chimwemwe
Tidzamkomana,
Pakufika Ambuye.

Alinkudza Ambuye Yesu,
Wakuphedwa pa dziko;
Alinkudza kukhala Mfumu,
Yoweruza mayiko.

Pakufika asonkhanitsa,
Anthu ake oyera;
Adzafuna mitundu yonse,
Omwe Iye ‘nafera.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 796 Timvere Mawu anu
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version