Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

 

ALINKUDZA wansoni Munthu,
Wakukhala Kumwamba;
Alinkudza m’ulemerero,
Ndi Mwamuna wa mtanda.

Aleluya, Aleluya,
Alinkudza kwa ife;
Ndi chimwemwe
Tidzamkomana,
Pakufika Ambuye.

Alinkudza Ambuye Yesu,
Wakuphedwa pa dziko;
Alinkudza kukhala Mfumu,
Yoweruza mayiko.

Pakufika asonkhanitsa,
Anthu ake oyera;
Adzafuna mitundu yonse,
Omwe Iye ‘nafera.

Post navigation

Previous: Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
Next: Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version