Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,

 

MMENE Yesu adzabwera,
Adza ndi mitambo;
Ndipo diso lililonse,
Lidzamuwona Iye.

Adza, adza,
Adza ndi mitambo,
Ndipo diso lililonse;
Lidzamuwona Iye.

Adzakhala pa chimpando,
Choweruziracho;
Nadzayamba kuweruza,
Milandu ya anthu’fe.

Angelo ‘dzagwira ntchito,
Yolekanitsadi;
Anthu onse a padziko,
M’magulu awiritu.

Olugama nadzayima,
Kudzanja lamanja;
Koma onse oyipawo,
Mbali yakumanzere.

Akudzanja lamanjalo,
Kumoyo wosatha;
Akudzanja lamanzere,
Kumoto Wosathawo.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version