Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

 

LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
Tamvani nyimbo za ‘mithenga aKumwambako;
Nafenso pansipa
Tim’yamikire ’Ye,
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera kalero.

Lambira Yesuyo,
Wokonda tonsefe;
Mabala ake achikondi awonekabe;
Tisayiwale ’yi
Zoŵaŵa zakezo,
Tileke kum’chimwira, kum’sautsa Yesuyo.

Lambira Yesuyo,
Uthenga wakewu
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko munomo:
Amaiŵala za
Kudana kwawoko,
Nayamikira Mfumu yamtendere monsemo.

Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi:
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi mitamboyi;
Tikweze dzinalo
La Mbuye Yesuyo,
Tim’yamikire pansi pano ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version