Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

 

LERO Kristu anauka,
Aleluya.
Ndilo tsiku lokondwera.
Aleluya.
Iye kale anafera,
Aleluya.
Nawombola otaika,
Aleluya.

Timwimbire zomtamanda
Aleluya.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Aleluya.
Natsikira kumanda,
Aleluya.
Nalanditsa akuipa.
Aleluya

Koma masauko ake,
Aleluya.
Anatiwombola ife.
Aleluya.
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Aleluya.
Mwana ndithu wa Mulungu.
Aleluya.

Timwimbire Mulungu wathu,
Aleluya.
Kuti atikonda ndithu:
Aleluya.
Mtamenso angelo inu,
Aleluya.
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Aleluya.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version