Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

  1. Home   »  
  2. Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

 

LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Lemekeza Mulungu Mwana,
Lemekeza Mulungu Mzimu,
Mulungu Mmodzi ndi wamkulu,
Lemekeza, lemekeza
Mulungu wathu yemweyo.

Mlemekeze, anakonda
Natitsuka m’mtima mwathu;
Anatiwombola ife
Tikakhale ndi chifumu.
Lemekeza, lemekeza
Yesu Mbuye Nsembeyo.

Lemekeza Mfumu yathu,
Mfumu ya mipingo yonse,
Ipambana anthu onse
Akumwamba ndi apansi.
Lemekeza, lemekeza
Mfumu ya mafumuyo

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version