Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

  1. Home   »  
  2. Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

 

TIYENI, dzalireni nane,
Tidze ku mtanda wa Ambuye,
Tionse tichitetu maliro;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Kodi misozi itisoŵa,
Poona anthu amanyoza?
Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Anena mawu m’mtanda momwe
Mawu ochepa achifundo,
Apempherera ’dani ake;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Ona chikondi cha Mulungu,
Ona zoipazo za anthu,
Koma chakula ndi chikondi;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version