Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

 

PANTHAWI yakufa Ambuye,
Anthu ananena:
“Dzipulumutsetu pamtandapo.”

(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O) Anafuula;
(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O)Anafuula;
“Eloyi, Eloyi
Mulungu wanga,
Mwandisiiranji,
Mwandisiiranji?”

Imfa ya Bwenzi lathu Yesu,
Yomvetsa chisoni;
Ophunzira onse anathaŵa.

Pamene anakhomedwatu,
Pamtanda Yesuyo;
Zoipa zathu zinam’psinja ‘Ye.

Imfa yake ndi yopambana,
Yotipulumutsa;
Yotitengera ife mtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version