Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
Next: Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1617 Anadzuka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version