Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version