Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

 

MLUNGU, Inutu,
Mwalenga dzuŵali,
Nyenyezi, mwezi mbee,
Ndi dzikoli.

Koma ineyu
Simuiŵala ’yi;
Mundisamala ’ne
Ndisagwe ’yi.

Mbuye, Msungi ’Nu,
Mutuma indedi
Za moyo wangawu
Zokomazi.

Yesu Mwanatu
Anafa imfayo
Achotsa zoti bii;
Nadzukanso;

Kuti m’Mwambamo
Ndikatamandetu
Wondisamalabe,
Mbuyangayu.

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version