Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

  1. Home   »  
  2. Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

 

MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
Ndi mtima wokondwera kuloŵa m’nyumbayi;
Chifukwa cha zabwino mwatichitirazi
Tikukuyamikirani leroli.

Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
Mwatimangira ’fe kuno kachisi wanuyu!
Ndi ulemerero wanu mudzaze m’nyumbayi;
Muyeretse, mudalitse munomu.

Tikondwa tonse ndikukuthokozani ’Nu
Poyamba kupemphera ndikuimbira ’mu;
Mommuno nsiku zonse mukhale nafetu,
Monga ndi angelo anu m’Mwambamo.

Ikhale ngati nyali yoŵala nyumbayi,
Yakutsogoza onse ophunthwa m’mdima bii;
Akunja ndi Akristu m’ŵapulumutse ndi
Kuunika kotuluka munomu.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version