Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 431 AKAPANDA kumanga,

 

AKAPANDA kumanga,
Nyumba Yehovayo;
Woyimanga nyumbayo,
Angomanga chabe.

Gwirani ntchito yake,
Ndi mapemphero;
Kuti Yehova adalitse,
Ntchito yanu.

Ngati mugwira ntchito,
Ndi nzeru zanuzo;
Mulibe phindu ndithu,
Pamaso pa Mbuye.

Tipempha ‘Nu Yehova,
M’dalitsetu ntchito;
Zathu kuti Ufumu,
Wanu Ukwezedwe.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version