Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version