Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,

 

DZIKO lonse lapansi,
Linachimwa kwa Mlungu,
Chilango chake ndicho cha imfa;
Koma podza Yesuyo,
Anathetsa mlanduwo;
Potifera ife pamtandapo.

Onani,
Mwana wa Nkhosa,
Wachotsa tchimo lonse pansipa;
Ndiye Yesu Mfumuyo,
Ndiye Mpulumutsiyo;
Wotifera ife pamtandapo.

Tsono mmene tadziwa,
Kuti ndife ochimwa,
Tiyeni tinke kwa Ambuyewo;
Tisachite manyazi,
Tiwauze tchimolo;
Iwo adzatikhululukira.

Wotikhululukira,
Adzatiwuza tonse,
Kuti tisadzachimwenso ndithu;
Zakale zatha ndithu,
Zatsala zatsopano;
Tasamba mwazi wake tayera.

Post navigation

Previous: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
Next: Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version