Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 412 MOYO uli pafupi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 412 MOYO uli pafupi,

Hymn 412 MOYO uli pafupi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 412 MOYO uli pafupi,

 

MOYO uli pafupi,
Monga kugwa kwa tsamba,
Ndikumanga mitolo kangaza;
Usachedwe m’zoipa,
Sudzapeza mpumulo;
Ndipo sadzakuyankha,
Kangaza.

Kangaza, kangazatu,
Yesu ali kuyitana, kangaza;
Usachedwe m’zoipa,
Sudzapeza mpumulo;
Ndipo sadzakuyankha,
Kangaza.

Unyamata ngovuta,
Umabwera nupita,
Ndipo sadzakuyankha kangaza;
Usachedwe m’zoipa,
Sudzapeza mpumulo;
Ndipo sadzakuyankha
Kangaza.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version