Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

  1. Home   »  
  2. Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

 

TIIMBE ndi kulalikira
Mthenga wa chikondicho
Anamva Mlungu m’Mwambamo
Kulira kwathu pansipa.

(Ndikhulupirira Yesu
Wobadwira m’kholamo;
Iye ndiye Mfumu yathu,
Timtame nthaŵi zonse.)

Kwa ife lero anabadwa
Mwana wa Mariyayo,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma
Mwini dziko lonseli.

Anadza nazo mphatso zake
Anatikonzeratu; Anatitseguliradi
Pakhome pa Ufumuwo.

Ambuye takutamandani
Tsiku lakubadwali,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Tiseke tonsefe.

A! Yesu Mbuye wakuyera,
Munagona m’kholamo;
Mudzikonzere leronso
Mogona m’mtima mwangamu.

Ulemerero m’Mwambamwamba
Ndi mtendere pansipa;
Tiimbe nafe nyimboyi,
Timyamikire Mbuyathu

(Yesu ndiye Mfumu,
Yesu ndiye Mfumu!
Ndikhulupirira Yesu wobadwira m’kholamo.)

Post navigation

Previous: Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
Next: Hymn 456 ANA inu, ana inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version