Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

  1. Home   »  
  2. Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

 

TIIMBE ndi kulalikira
Mthenga wa chikondicho
Anamva Mlungu m’Mwambamo
Kulira kwathu pansipa.

(Ndikhulupirira Yesu
Wobadwira m’kholamo;
Iye ndiye Mfumu yathu,
Timtame nthaŵi zonse.)

Kwa ife lero anabadwa
Mwana wa Mariyayo,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma
Mwini dziko lonseli.

Anadza nazo mphatso zake
Anatikonzeratu; Anatitseguliradi
Pakhome pa Ufumuwo.

Ambuye takutamandani
Tsiku lakubadwali,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Tiseke tonsefe.

A! Yesu Mbuye wakuyera,
Munagona m’kholamo;
Mudzikonzere leronso
Mogona m’mtima mwangamu.

Ulemerero m’Mwambamwamba
Ndi mtendere pansipa;
Tiimbe nafe nyimboyi,
Timyamikire Mbuyathu

(Yesu ndiye Mfumu,
Yesu ndiye Mfumu!
Ndikhulupirira Yesu wobadwira m’kholamo.)

Post navigation

Previous: Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
Next: Hymn 456 ANA inu, ana inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version