Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

 

MAWU akewo anamveka ponse,
Olalikidwa ndi aneneriwo;
Kuti yense wakumvera mawuwo,
Apulumuke.

(Mawuwo) Amveke,
(Tu) Kwa onsewo;
(Wo) Muetseratu ‘we sadzafa ndithu.

Tamveratu ‘we Mawu a Mulungu,
Khulupilira mwa
Ambuye Yesu;
Udzalandira moyo wosathawo,
Udzakondwera.

Tsoka kwa iye wosakhulupira,
Zolalikidwa ndi aneneriwo;
Koma patsiku la chiŵeruziro,
Adzafa ndithu

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version