Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version