Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

 

MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa;
Ndilibe wina wakundithandiza,
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

Kamoyo kanga katha lero lino,
Zidzachokanso zinthuzo za dziko;
Zimasinthika zonse zooneka,
Simusi nthika, mkhale ndinutu.

Koma kalelo mnakhalitsa pano,
Mukhale ndine, msandichokerenso,
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
Komatu mukhalitse ndinetu.

E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Usiku, msana, mkhale ndinetu.

Adani sindiopa mukalipo
Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version