Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

 

MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa;
Ndilibe wina wakundithandiza,
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

Kamoyo kanga katha lero lino,
Zidzachokanso zinthuzo za dziko;
Zimasinthika zonse zooneka,
Simusi nthika, mkhale ndinutu.

Koma kalelo mnakhalitsa pano,
Mukhale ndine, msandichokerenso,
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
Komatu mukhalitse ndinetu.

E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Usiku, msana, mkhale ndinetu.

Adani sindiopa mukalipo
Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.

Post navigation

Previous: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
Next: Hymn 363 ATATE ndiyamika,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version