Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

  1. Home   »  
  2. Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

 

PEMPHERO ndiko kufuna,
Kulakalakatu;
Ndi monga moto liyaka
Mumtima wa munthu.

Pemphero ndiko kulira,
Ngakhale misozi,
Kupenyetsetsa Kumwamba,
Mulungu mpafupi.

Pemphero ndiko kufuna
Kwa mwana wamng’ono;
Ndiponso mawu amphamvu
A munthu wamvanu.

Pemphero ndiwo mweyawo
Apuma akristu;
Ndi mapemphero tiloŵa
Dziko la imfalo.

Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Kupempha kotero,
Kuyandikira kwa Mlungu
Ndi mtima wabwino.

Post navigation

Previous: Hymn 345 ATATE, ndipempha
Next: Hymn 347 YESU, ndipemphera

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version