Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

 

’TATE wa Kumwambako,
Likayere Dzinalo,
Udzetu Ufumu wanu;
Chifuniro chanucho
Chichitike pansipa
Monga chachitika kwanu.

Mutipatse leroli
E, chakudya chathuchi
Tsiku n’tsiku tichilira.
Mukhululukiredi
Tchimo lathu, monga ’fe
Iwo adatichimwira.

Musatifikitsemo
Muli mayeserowo,
Koma mutipulumutse.
Wanu ndi ufumuwo,
Mphamvu ndi ulemunso
Kufikira nthaŵi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version