Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

  1. Home   »  
  2. Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

 

PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala;
Mbuyathu Yesu wapitako,
Iye ’natsogola;
Tidzamtsatira ife tonse,
Tsiku lomaliza.

Tiyeni, tiyeni,
Ku dziko lakudala;
Tidzafikira m’dziko ilo
Tsiku lomaliza.

Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Atipulumutse.

Ulendo wathu ukadzatha
Tidzafika kwathu,
Adzatifitsa ife komwe
Yesu Mbuye wathu.
Sitidzapeza masautso
M’dziko la Mulungu,
Tidzakondwera chikondwere
Nthaŵi zathu zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
Next: Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version