Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

  1. Home   »  
  2. Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;

 

PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Komatu kwa Mulungu kuli
Dziko lakudala;
Mbuyathu Yesu wapitako,
Iye ’natsogola;
Tidzamtsatira ife tonse,
Tsiku lomaliza.

Tiyeni, tiyeni,
Ku dziko lakudala;
Tidzafikira m’dziko ilo
Tsiku lomaliza.

Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphere Mbuye wathu,
Atipulumutse.

Ulendo wathu ukadzatha
Tidzafika kwathu,
Adzatifitsa ife komwe
Yesu Mbuye wathu.
Sitidzapeza masautso
M’dziko la Mulungu,
Tidzakondwera chikondwere
Nthaŵi zathu zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version