Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

 

NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namachereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.

Mulungu wanga ndiye wachifundo
Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
Apulumutsa anthu akufoka,
Akathandiza nkhaŵa imachoka.

Mtimanga, bwera kuti upumule,
Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Ndingakhumudwe asungira phazi.

Nditani ine kubwezera Mbuye
Zokoma zonse anandichitira?
Chipulumutso chake ndidzatama,
Ndinalumbira zija ndidzapatsa.

Imfa ya anthu ake imkomera,
Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.

Post navigation

Previous: Hymn 319 NDIDZATANI ine,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version