Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

 

NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namachereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.

Mulungu wanga ndiye wachifundo
Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
Apulumutsa anthu akufoka,
Akathandiza nkhaŵa imachoka.

Mtimanga, bwera kuti upumule,
Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Ndingakhumudwe asungira phazi.

Nditani ine kubwezera Mbuye
Zokoma zonse anandichitira?
Chipulumutso chake ndidzatama,
Ndinalumbira zija ndidzapatsa.

Imfa ya anthu ake imkomera,
Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version