Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

 

AKRISTU limbikani,
Imani mtima nji!
Mbendera nyamulani,
Msatenthemere ’yi.
Wotsogolera wathu
Ndi Mwana wa Mulungu;
Adzagonjetsa onse
Adani athuwo.

Tigwire nkhondo yomwe
Ya Mbuye wathuyo;
Tileke zakuipa
Zokhala m’mtimamo.
Sitikwanira tokha
Kuleka zathu zomwe,
Koma Mbuyathu Yesu
Atithangatatu.

Tsopano timenyana
Ndi zakuipazi;
Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
Yesu adzalandira
Ankhondo ake onse;
Adzakhalika naye
Kumwamba komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version